Masalmo 119:115-118 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

115. Mundicokere ocita zoipa inu;Kuti ndisunge malamulo a Mulungu wanga.

116. Mundicirikize monga mwa mau anu, kuti ndikhale ndi moyo;Ndipo ndisacite manyazi pa ciyembekezo canga.

117. Mundigwirizize ndipo ndidzapulumutsidwa,Ndipo ndidzasamalira malemba anu cisamalire.

118. Mupepulaonseakusokeram'malemba anu;Popeza cinyengo cao ndi bodza.

Masalmo 119