Masalmo 115:17-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Akufa salemekeza Yehova,Kapena ali yense wakutsikira kuli cete:

18. Koma ife tidzalemekeza YehovaKuyambira tsopano kufikira nthawi yonse.Haleluya.

Masalmo 115