3. Citurukire dzuwa kufikira kulowa kwaceLilemekezedwe dzina la Yehova.
4. Yehova akwezeka pamwamba pa amitundu onse,Ulemerero wace pamwambamwamba.
5. Akunga Yehova Mulungu wathu ndani?Amene akhala pamwamba patali,
6. Nadzicepetsa apenyeZam'mwamba ndi za pa dziko lapansi.
7. Amene autsa wosauka lrumcotsa kupfumbi,Nakweza waumphawi kumcotsa kudzala.