Masalmo 110:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Yehova walamulira, ndipo sadzasintha,Inu ndinu wansembe kosathaMonga mwa cilongosoko ca Melikizedeke.

5. Yehova pa dzanja lamanja lakoAdzaphwanya mafumu tsiku la mkwiyo wace.

6. Adzaweruza mwa amitundu,Adzadzaza dziko ndi mitembo;Adzaphwanya mitu m'maiko ambiri.

7. Adzamwa ku mtsinje wa panjira;Cifukwa cace adzaweramutsa mutu wace.

Masalmo 110