Masalmo 106:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Talakwa pamodzi ndi makolo athu;Tacita mphulupulu, tacita coipa.

7. Makolo athu sanadziwitsa zodabwiza zanu m'Aigupto;Sanakumbukila zacifundo zanu zaunyinji;Koma anapikisana ndi Inu kunyanja, ku Nyanja Yofiira.

8. Koma anawapulumutsa cifukwa ca dzina lace,Kuti adziwitse cimphamvu cace.

Masalmo 106