Masalmo 106:32-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. Anautsanso mkwiyo wace ku madzi a Meriba,Ndipo kudaipira Mose cifukwa ca iwowa:

33. Pakuti anawawitsa mzimu wace,Ndipo analankhula zosayenera ndi milomo yace.

34. Sanaononga mitunduyo ya anthu,Imene Mulungu adawauza;

35. Koma anasokonekerana nao amitundu,Naphunzira nchito zao:

Masalmo 106