5. Cifukwa ca liu la kubuula kwangaMnofu wanga umamatika ku mafupa anga.
6. Ndikunga bvuwo m'cipululu;Ndikhala ngati kadzidzi wa kumabwinja.
7. Ndidikira, ndikhala ngati mbawaIri yokha pamwamba pa tsindwi.
8. Adani anga anditonza tsiku lonse;Akundiyarukirawo alumbirira ine.
9. Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate,Ndi kusanganiza-comwera canga ndi misozi,