Marko 7:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

9. Ndipo ananena nao, Bwino mukaniza lamulo la Mulungu, kuti musunge mwambo wanu,

10. Pakuti Mose anati, Lemekeza atate wako ndi amako; ndipo iye wakunenera zotpa atate wace kapena amai wace, afe ndithu;

Marko 7