Maliro 3:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ine ndine munthuyu wakuona msauko ndi ndodo ya ukali wace.

2. Wanditsogolera, nandiyendetsa mumdima, si m'kuunika ai.

3. Zoonadi amandibwezera-bwezera dzanja lace monditsutsa tsiku lonse.

4. Wagugitsa thupi langa ndi khungu langa, natyola mafupa anga.

Maliro 3