Malaki 3:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kuyambira masiku a makolo anu mwapambuka kuleka malemba anga osawasunga. Bwererani kudza kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu, ati Yehova wa makamu. Koma inu mukuti, Tibwerere motani?

Malaki 3

Malaki 3:3-8