38. Ndipo m'mene anakhuta, anapepuza ngalawa, nataya tirigu m'nyarija.
39. Ndipo kutaca sanazindikira dzikolo; koma anaona pali bondo la mcenga; kumeneko anafuna, ngati nkutheka, kuyendetsako ngalawa.
40. Ndipo m'mene anataya anangula anawasiya m'nyanja, namasulanso zingwe zomanga tsigiro; ndipo pokweza thanga la kulikuru, analunjikitsa kumcenga.
41. Koma pofika pamalo pokomana mafunde awiri, anatsamitsapo ngalawa; ndipo kulikuru kunatsama, ndi kukhala kosasunthika, koma kumakaliro kunasweka ndi mphamvu ya mafunde.
42. Ndipo uphungu wa asilikari udati awapheandende, angasambire, ndi kuthawa.