Macitidwe 14:25-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Ndipo atalankhula mau m'Perge, anatsikira ku Ataliya;

26. komweko anacoka m'ngalawa kunka ku Antiokeya, kumene anaikizidwa ku cisomo ca Mulungu ku Ilchito imene adaimarizayo,

27. Pamene anafika nasonkhanitsa Mpingo anabwerezanso zomwe Mulungu anacita nao, kuti anatsegulira amitundu pa khomo la cikhulupiriro.

28. Ndipo anakhala pamenepo ndi akuphunzira nthawi yaikuru.

Macitidwe 14