Luka 17:32-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. Kumbukilani mkazi wa Loti,

33. iye ali yense akafuna kusunga moyo wace adzautaya, koma iye ali yense akautaya, adzausunga.

34. Ndinena ndi inu, usiku womwewo adzakhala awiri pa kama mmodzi; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

35. Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa. [

36. ]

37. Ndipo anayankha nanena kwa iye, Kuti, Ambuye? Ndipo anati kwa iwo, Pamene pali mtembo, pomweponso miimba idzasonkhanidwa.

Luka 17