Luka 17:18-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Akubwera kulemekeza Mulungu sanapezeka mmodzi kodi, koma mlendo uyu?

19. Ndipo anati kwa iye, Nyamuka, nupite; cikhulupiriro cako cakupulumutsa iwe.

20. Ndipo pamene Afarisi anamfunsa iye, kuti, Ufumu wa Mulungu ukudza liti, anawayarikha, nati, Ufumu wa Mulungu sukudza ndi maonekedwe;

Luka 17