Levitiko 23:42-44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

42. Mukhale m'misasa masiku asanu ndi awiri; onse obadwa m'dziko mwa Israyeli akhale m'misasa;

43. kuti mibadwo yanu ikadziwe lruti ndinakhalitsa ana a Israyeli m'misasa, pamene ndinawaturutsa m'dziko la Aigupto; Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

44. Ndipo Mose anafotokozera ana a Israyeli nyengo zoikika za Yehova.

Levitiko 23