Levitiko 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ubwere nayo nsembe yaufa yopangika ndi izi kwa Yehova; ndipo atabwera naco kwa wansembe, iyeyo apite naco ku guwa la nsembe.

Levitiko 2

Levitiko 2:1-15