Hagai 2:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ulemerero wotsiriza wa nyumba iyi udzaposa woyambawo, ati Yehova wa makamu; ndipo m'malo muno ndidzapatsa mtendere, ati Yehova wa makamu.

Hagai 2

Hagai 2:7-19