Genesis 7:22-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. zonse zimene m'mphuno zao munali mpweya wa maimu wa moyo, zonse zinali pamtunda, zinafa.

23. Ndipo zinaonongedwa zamoyo zimene zonse zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dzikolapansi: anatsala Nowayekha ndi amene anali pamodzi naye m'cingalawa.

24. Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Genesis 7