Genesis 46:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi ana amuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana amuna a Perezi ndiwo Hezroni ndi Hamuli.

Genesis 46

Genesis 46:3-21