Genesis 29:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali m'mamawa, anaona kuti ndi Leya; ndipo anati kwa Labani, Ciani wandicitira ine? Kodi sindinakutumikira iwe cifukwa ca Rakele? wandinyenga ine bwanji?

Genesis 29

Genesis 29:16-27