Genesis 21:33-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Ndipo Abrahamu ananka mtengo wabwemba pa Beereseba, naitanira pamenepo dzina la Yehova, Mulungu wa nthawi zonse.

34. Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti.

Genesis 21