Ezekieli 36:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzati, Dziko ili lacipululu lasanduka ngati munda wa Edene, ndi midzi yamabwinja, ndi yacipululu, ndi yopasuka, yamangidwa malinga, muli anthu m'mwemo.

Ezekieli 36

Ezekieli 36:32-36