Ezekieli 20:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinati kwa ana ao m'cipululu, Musamayenda m'malemba a atate anu, musawasunga maweruzo ao, kapena kudzidetsa ndi mafano ao;

Ezekieli 20

Ezekieli 20:17-26