Ezekieli 14:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pamenepo anafika kwa ine akulu ena a Israyeli nakhala pansi pamaso panga.

2. Ndipo anandidzera mau a Yehova, akuti,

3. Wobadwa ndi munthu iwe, anthu awa anautsa mafano ao mumtima mwao, naimika cokhumudwitsa ca mphulupulu yao pamaso pao; ndifunsidwe nao konse kodi?

Ezekieli 14