26. Ana a Rama ndi Gaba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.
27. Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.
28. Anthu a ku Beteli ndi Ai, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
29. Ana a Nebo, makumi asanu mphambu awiri.