Ezara 2:26-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ana a Rama ndi Gaba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

27. Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

28. Anthu a ku Beteli ndi Ai, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.

29. Ana a Nebo, makumi asanu mphambu awiri.

Ezara 2