22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.
23. Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.
24. Ana a Azimaveti, makumi anai mphambu awiri.
25. Ana a Kiriyati Arimu, Kefira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.
26. Ana a Rama ndi Gaba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.