Deuteronomo 28:28-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Yehova adzakukanthani ndi misala, ndi khungu, ndi kuzizwa mumtima;

29. ndipo mudzafufuza usana, monga wakhungu amafufuza mumdima, ndipo simudzapindula nazo njira zanu; koma mudzakhala wopsinjika, nadzakuberani masiku onse, wopanda wina wakukupulumutsani.

30. Mudzaparana ubwenzi ndi mkazi, koma mwamuna wina adzagona naye; mudzamanga nyumba, osakhala m'mwemo; mudzanka munda wamphesa, osalawa zipatso zace.

Deuteronomo 28