Aroma 15:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ine ndekhanso, abale anga, nditsimikiza mtima za inu, kuti inu nokhanso muli odzala ndi ubwino, odzazidwa ndi kudziwitsa konse, ndi kukhoza kudandaulirana wina ndi mnzace.

Aroma 15

Aroma 15:6-19