10. pakuti ndi mtima munthu akhulupira kutengapo cilungamo; ndi m'kamwa abvomereza kutengapo cipulumutso
11. Pakuti lembo litere, Amene ali yense akhulupirira iye, sadzacita manyazi.
12. Pakuti kulibe kusiyana Myuda ndi Mhelene; pakuti Yemweyo ali Ambuye wa onse, nawacitira zolemera onse amene aitana pa iye;
13. pakuti, amene ali yense adzaitana pa dzina la Ambuye adzapulumuka.