Aroma 10:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. pakuti ndi mtima munthu akhulupira kutengapo cilungamo; ndi m'kamwa abvomereza kutengapo cipulumutso

11. Pakuti lembo litere, Amene ali yense akhulupirira iye, sadzacita manyazi.

12. Pakuti kulibe kusiyana Myuda ndi Mhelene; pakuti Yemweyo ali Ambuye wa onse, nawacitira zolemera onse amene aitana pa iye;

13. pakuti, amene ali yense adzaitana pa dzina la Ambuye adzapulumuka.

Aroma 10