Aefeso 5:30-33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. pakuti tiri ziwalo za thupi lace.

31. 1 Cifukwa ca ici munthu azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wace; ndipo iwo awiri adzakhala thupi limodzi.

32. Cinsinsi ici ncacikuru; koma ndinena ine za Kristu ndi Eklesia.

33. Komanso inu, yense pa yekha, yense akonde mkazi wace wa iye yekha, monga adzikonda yekha; ndipo 2 mkaziyo akumbukile kuti aziopa mwamuna.

Aefeso 5