3 Yohane 1:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. pakuti cifukwa ca dzinali anaturuka, osalandira kanthu kwa amitundu.

8. Cifukwa cace ife tiyenera kulandira otere, kuti tikakhale othandizana naco coonadi,

9. Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkuru wa iwo, satilandira ife.

3 Yohane 1