2 Samueli 8:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anamveketsa dzina lace pamene anabwera uko adakantha Aaramu m'cigwa ca mcere, ndiwo anthu zikwi khumi mphambu zisanu ndi zitatu.

2 Samueli 8

2 Samueli 8:12-18