2 Samueli 5:14-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Maina a iwo anambadwira m'Yerusalemu ndi awa: Samua, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomo,

15. ndi Ibara ndi Elisua, ndi Nefegi ndi Yafiya;

16. ndi Elisama ndi Eliada ndi Elifeleti.

17. Koma pamene Afilisti anamva kuti adamdzoza Davide mfumu ya Israyeli, Afilisti onse anakwera kukafuna Davide; ndipo Davide anacimva natsikira kungaka kuja.

2 Samueli 5