23. Ndipo Yoabu anali woyang'anira khamu lonse la Israyeli; ndi Benaya, mwana wa Jehoyada, anayang'anira Akereti ndi Apeleti;
24. ndi Adoramu anayang'anira msonkho; ndi Jehosafati mwana wa Ahiludi anali wolemba mbiri;
25. ndi Seva anali mlembi; ndi Zadoki ndi Abyatara anali ansembe;
26. ndiponso Ira Mjairi anali nduna ya Davide.