2 Samueli 19:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu inanyamuka, nikakhala pacipata, Ndipo inauza anthu kuti, Onani mfumu irikukhala pacipata; anthu onse nadza pamaso pa mfumu. Koma Aisrayeli adathawa, munthu yense ku hema wace.

2 Samueli 19

2 Samueli 19:4-15