2 Mbiri 11:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo atafika ku Yerusalemu Rehabiamu, anamemeza a nyumba ya Yuda ndi Benjamini amuna osankhika zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu, ndiwo ankhondo, alimbane ndi Aisrayeli kubwezanso ufumu kwa Rehabiamu.

2. Koma mau a Yehova anadza kwa Semaya munthu wa Mulunguyo, ndi kuti,

3. Lankhula ndi Rehabiamu mwana wa Solomo mfumu ya Yuda ndi Benjamini, ndi kuti,

2 Mbiri 11