2 Mafumu 9:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata ace anamnyamulira pagareta kumka naye ku Yerusalemu, namuika ku manda ace pamodzi ndi makolo ace m'mudzi wa Davide.

2 Mafumu 9

2 Mafumu 9:25-34