2 Mafumu 5:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Namani anati, Mukakana, andipatse akatundu a dothi osenza nyuru ziwiri; pakuti mnyamata wanu sadzaperekanso nsembe yopsereza kapena yophera kwa milungu yina, koma kwa Yehova.

2 Mafumu 5

2 Mafumu 5:9-26