2 Mafumu 24:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yoyakini anali wa zaka khumi mphambu zisanu ndi zitatu polowa iye ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu miyezi itatu; ndi dzina la mace ndiye Nehusita mwana wa Elinatani wa ku Yerusalemu.

2 Mafumu 24

2 Mafumu 24:5-18