2 Mafumu 19:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Yehova za mfumu ya Asuri, iye sadzalowa m'mudzi muno, kapena kuponyamo mubvi, kapena kufikako ndi cikopa, kapena kuundira mtumbira.

2 Mafumu 19

2 Mafumu 19:24-37