2 Mafumu 11:20-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Nakondwerera anthu onse a m'dziko, ndi m'mudzi munali phe; ndipo adapha Ataliya ndi lupanga ku nyumba ya mfumu.

21. Yoasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa iye ufumu.

2 Mafumu 11