13. Kama inu, abale, musaleme pakucita zabwino.
14. Koma ngati wina samvera mau athu m'kalata uyu, yang'anirani ameneyo, kuti musayanjane naye, kuti acite manyazi.
15. Koma musamuyese mdani, kama mumuyambirire ngati mbale.
16. Ndipo Ambuye wa mtendere yekha atipatse ife mtendere nthawi zonse, monsemo. Ambuye akhale ndi inu nonse.