2 Akorinto 4:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

popeza sitipenyerera zinthu zooneka, koma zinthu zosaoneka; pakuti zinthu zooneka ziri za nthawi, koma zinthu zosaoneka ziri zosatha.

2 Akorinto 4

2 Akorinto 4:11-18