2 Akorinto 2:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti m'cisautso cambiri ndi kuwawa mtima ndinalembera inu ndi misozi yambiri; si kuti ndikumvetseni cisoni, koma kuti mukadziwe cikondi ca kwa inu, cimene ndiri naco koposa.

2 Akorinto 2

2 Akorinto 2:1-5