1 Samueli 5:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali atafika nalo, dzanja la Yehova linatsutsa mudziwo ndi kusautsa kwakukuru; ndipo anazunza anthu a mudziwo, akuru ndi ang'ono; ndi mafundo anawabuka.

1 Samueli 5

1 Samueli 5:1-12