1 Samueli 29:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Akisi anayankha nanena ndi Davide, Ndidziwa kuti pamaso panga uli wabwino, ngati mthenga wa Mulungu; koma akalonga a Afilisti anena, iye asamuke nafe kunkhondoko.

1 Samueli 29

1 Samueli 29:1-11