1 Samueli 13:20-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. koma Aisrayeli onse adafotsikira kwa Afilisti, kuti awasaniire munthu yense cikhasu cace, colimira cace, nkhwangwa yace, ndi khasu lace;

21. koma analf nao matupa kukonza makasu, ndi zikhasu ndi makasu a mana ndi nkhwangwazo; ndi kusongola zothwikira.

22. Comweco kunali kuti tsiku lankhondolo sunapezeka mkondo kapena lupanga m'manja a anthu onse anali ndi Sauli ndi Jonatani; koma Sauli yekha ndi Jonatani mwana wace anali nazo.

23. Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anaturuka kunka ku mpata wa ku Mikimasi.

1 Samueli 13