1 Petro 3:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Kristunso adamva zowawa kamodzi, cifukwa ca macimo, wolungama m'malo mwa osalungama, kuti akatifikitse kwa Mulungu; wophedwatu m'thupi, koma woparsidwa moyo mumzimu;

1 Petro 3

1 Petro 3:13-22