1 Mbiri 6:55-59 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

55. kwa iwo anapereka Hebroni m'dziko la Yuda, ndi podyetsa pace pozungulira pace;

56. koma minda ya mudzi ndi miraga yace anapatsa Kalebi mwana wa Yefune.

57. Ndi kwa ana a Aroni anapereka midzi yopulumukirako: Hebroni, ndi Libina ndi mabusa ace, ndi Yatiri, ndi Esitemowa ndi mabusa ace,

58. ndi Hileni ndi mabusa ace, ndi Debiri ndi mabusa ace,

59. ndi Asani ndi mabusa ace, ndi Betesemesi ndi mabusa ace;

1 Mbiri 6