1 Mbiri 4:22-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. ndi Yokimu, ndi amuna a Kozeba, ndi Yoasi, ndi Sarafa wolamulira m'Moabu, ndi Yasubilehemu; koma mau awa ndiwo a kale lomwe.

23. Iwo ndiwo oumba mbiya, ndi okhala m'Netaimu, ndi m'Gedera; anakhala komweko ndi mfumu m'nchito yace.

24. Ana a Simeoni: Nemueli, ndi Yamini, Yaribi, Zera, Sauli,

25. Salumu mwana wace, Mibsamu mwana wace, Misma mwana wace.

1 Mbiri 4